Malawi Voice PRESIDENTIAL DEBATE IKADAKOMA IYI!!! HOST: - TopicsExpress



          

Malawi Voice PRESIDENTIAL DEBATE IKADAKOMA IYI!!! HOST: Mention five things the Government has done to improve the lives of Malawians JB: I wont mention them. Malawians know kuti nzotheka HOST:You claim the economy has improved yet prices of basic goods have increased by 150% since you became President. Would you care to explain this? JB:Mwafunsa chifukwa ndine mzimayi? Sindisiyabe kuyenda ndikupeleka ngombe, mbudzi ndi bakha HOST:Bingu introduced the Zero Deficit Budget and you have followed the same route. Why? JB:Azungu anena. Ine ndikadatani? Koma sumukuwona kuti MA spelling ndiwosiyana zoona!? Koma AMalawi anzanga siyani nkhanza kwa Amayi chonde chonde! HOST:Cashgate is one of the key electoral issues in terms of curbing corruption. Additionally, there are allegations of corruption related to your parties acquisition of maize which you continue to distribute? What are your sources of income and why havent you as leader set an example by declaring your assets? JB:Ndinayamba kale kale kutakata. Mandazi Ndi gain yotentha. A Malawi tulo koma! Ndazi imodzi matumba a chimanga khumi. Chodabwitsa Ndi chiani apa HOST:And now the issue of Lake MALAWI... JB:Iiiiiiiiiii mafunso onsewa ndiyankhe ndekha HOST:You represent Malawi. But your dressing appears to imitate Ellen Johnson Sirleaf.... JB:Now you are getting personal, Moderator.Iyayi!!!!! Panopa ndiye ndi kuyankha HOST:You have 1 minute JB:Aaaaaaa! A Helen Singh mwawapatsa 1 hour. Kukhala mzimayi sichifukwa!
Posted on: Mon, 21 Apr 2014 20:05:50 +0000

Trending Topics



Recently Viewed Topics




© 2015