Boy: jucha kodi abamu yako ituluka liti? Jucha: aaa pa 20 july - TopicsExpress



          

Boy: jucha kodi abamu yako ituluka liti? Jucha: aaa pa 20 july koma ma cd alipo ngati mukuwafuna man Boy: oky zabwino nde sista wako ali kutiko? Jucha: alipo Boy: kodi user name yake ndi chani? Jucha:sindi matchula chapomba Boy:oky boss nde ma cd akowo utha kungo patsilaa mawa ku church akandipatsile? Jucha: azakhala pa khonde man mutha kuwapeza Boy: oky bro kodi paja uku khala kuti? Jucha: ndine batchala paja ku nancholi Boy: ooo oky nde akwanu? Jucha:kwa bambo ndi mayi chapomba Boy: kodi paja achapomba amakhala kuti? Jucha: ase ngati ukufuna mlongo wanga ungonena wamva zopusa ndimadana. Nazo kodi ndi intavyu yapa radio? Mafuso oseweo bwanji ufuna uzabe? Sista sista chani apa mxiew.. Kuyesana eti ifetu ndife akwabusa bible timalidziwa titha kukupatsa vesi yomwe timamenyela anthu wamvaaa? Samson sukumudziwa? Tikusungatu tsitsi wamvAaaaaaaaa mphamvu zathu zili mutsistsi
Posted on: Sat, 05 Jul 2014 17:09:33 +0000

Trending Topics



Recently Viewed Topics




© 2015