DONA YANGA IMANUNKHA ANYEZI KU MALISECHE KWAKE Through ths - TopicsExpress



          

DONA YANGA IMANUNKHA ANYEZI KU MALISECHE KWAKE Through ths page mundithandize ndine mmodzi mwamuna odziwa kukonda, koma kufika pofika kubwera pa public chonchi penapake sizilibwino. Ndakhala ndikufuna mkazi wa serious kwa nthawi yayitali ndipo ndidachitika mwayi dona ya ku mtima kwanga ndidakumana nayo pa shopryt ya ku Limbe, tonse titawonana tidangosekelelana kenaka tayamba kucheza ndikupasana ma number takhala ma week awiri tikulumikizaana pa lamya, kenaka ndinamuyitanira kwathu, monga muziwa sipamalephera kugwiranagwirana, timiromo patali patali mpaka malaya athu onse tinapezeka kuti tilibe. Chongomuchotsa underwear kunatuluka chifungo cha anyezi ku maliseche kwake, mpaka ndinangonamizira kuti mutu wangoyamba kundipweteka mpaka tinavala malaya. Realy wntd to talk to her about it that day koma ndinawopa kumuwuza kwake mpaka anapita kwawo. Akulu akulu mkaziyu ndimamukonda koma kununkha ngati anyezi kumaliseche ndi mauka, kapena matenda anji? Zikungondiopsa ineyo and how best can I help her without offending her.
Posted on: Thu, 05 Dec 2013 04:54:40 +0000

Trending Topics



Recently Viewed Topics




© 2015